Amosi 5:23 - Buku Lopatulika23 Mundichotsere phokoso la nyimbo zanu; sindifuna kumva mayimbidwe a zisakasa zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Mundichotsere phokoso la nyimbo zanu; sindifuna kumva mayimbidwe a zisakasa zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Musandisokose nazo nyimbo zanu zachipembedzo, sindingathe kupirira kulira kwa azeze anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Musandisokose nazo nyimbo zanu! Sindidzamvetsera kulira kwa azeze anu. Onani mutuwo |