Amosi 5:21 - Buku Lopatulika21 Ndidana nao, ndinyoza zikondwerero zanu, sindidzakondwera nayo misonkhano yanu yoletsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndidana nao, ndinyoza zikondwerero zanu, sindidzakondwera nao masonkhano anu oletsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Chauta akuti, “Masiku anu achikondwerero ndimadana nawo ndipo ndimaŵanyoza. Misonkhano yanu yachipembedzo siindikondwetsa konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza; sindikondwera nayo misonkhano yanu. Onani mutuwo |