Amosi 5:20 - Buku Lopatulika20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala la mdima, si la kuunika ai? Lakuda bii, lopanda kuwala m'menemo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala la mdima, si la kuunika ai? Lakuda bii, lopanda kuwala m'menemo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Kodi suja tsiku la Chauta ndi mdima wokhawokha osati kuŵala, kodi suja lili ngati usiku wabii wopanda mpoti mbee pomwe! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala, mdima wandiweyani, popanda powala pena paliponse? Onani mutuwo |