Amosi 5:18 - Buku Lopatulika18 Tsoka inu akufuna tsiku la Yehova? Mudzapindulanji nalo tsiku la Yehova? Ndilo mdima, si kuunika ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Tsoka inu akufuna tsiku la Yehova? Mudzapindulanji nalo tsiku la Yehova? Ndilo mdima, si kuunika ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsoka kwa inu amene mumalilakalaka tsiku la Chauta! Kodi tsiku limenelo lidzakupinduliraninji inuyo? Kudzakhalatu mdima, osati kuŵala ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Tsoka kwa inu amene mumalakalaka tsiku la Yehova! Chifukwa chiyani mumalakalaka tsiku la Yehova? Tsikulo kudzakhala mdima osati kuwala. Onani mutuwo |