Amosi 5:17 - Buku Lopatulika17 Ndi m'minda yonse yamipesa mudzakhala kulira, pakuti ndipita pakati pako, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndi m'minda yonse yamipesa mudzakhala kulira, pakuti ndipita pakati pako, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 M'minda yonse ya mphesa mudzakhala kulira kokhakokha, pakuti ndidzakulanganidi nonsenu.” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha, pakuti Ine ndidzadutsa pakati panu,” akutero Yehova. Onani mutuwo |