Amosi 5:14 - Buku Lopatulika14 Funani chokoma, si choipa ai; kuti mukhale ndi moyo; motero Yehova Mulungu wa makamu adzakhala ndi inu, monga munena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Funani chokoma, si choipa ai; kuti mukhale ndi moyo; motero Yehova Mulungu wa makamu adzakhala ndi inu, monga munena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Muike mtima pa zabwino osati pa zoipa, kuti mukhalebe ndi moyo. Apo Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse, adzakhala nanu monga mwaneneramo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa, kuti mukhale ndi moyo. Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu, monga mmene mumanenera kuti ali nanu. Onani mutuwo |