Amosi 5:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake wochenjerayo akhala chete nthawi yomweyo; pakuti ndiyo nthawi yoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake wochenjerayo akhala chete nthawi yomweyo; pakuti ndiyo nthawi yoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nchifukwa chake pa nthaŵi yotere munthu wanzeru salankhulapo kanthu, chifukwa ndi nthaŵi yoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu, popeza ndi nthawi yoyipa. Onani mutuwo |