Amosi 3:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ndidzakantha nyumba ya nyengo yachisanu, pamodzi ndi nyumba ya nyengo yadzuwa; ndi nyumba zaminyanga zidzaonongeka; ndi nyumba zazikuluzo zidzatha, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ndidzakantha nyumba ya nyengo yachisanu, pamodzi ndi nyumba zaminyanga zidzaonongeka; ndi nyumba zazikuluzo zidzatha, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndidzagwetseratu nyumba za nthaŵi yachisanu ndi za nthaŵi yamafundi. Nyumba zaminyanga zidzaonongeka, ndithu nyumba zazikulu zidzaphwasuka.” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndidzagwetsa nyumba ya pa nthawi yozizira pamodzi ndi nyumba ya pa nthawi yotentha; nyumba zokongoletsedwa ndi minyanga ya njovu zidzawonongedwa ndipo nyumba zikuluzikulu zidzaphwasulidwa,” akutero Yehova. Onani mutuwo |