Amosi 3:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti tsiku lakumlanga Israele chifukwa cha zolakwa zake, ndidzalanganso maguwa a nsembe a ku Betele; ndi nyanga za guwa la nsembe zidzadulidwa, ndipo zidzagwa pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti tsiku lakumlanga Israele chifukwa cha zolakwa zake, ndidzalanganso maguwa a nsembe a ku Betele; ndi nyanga za guwa la nsembe zidzadulidwa, nizidzagwa pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Pa tsiku limene ndidzalange Israele chifukwa cha zolakwa zake, maguwa a ku Betele ndidzaŵagumula, ndipo nyanga za guwa zidzathyoka nkugwa pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Pa tsiku limene ndidzalange Israeli chifukwa cha machimo ake, ndidzagumula maguwa ansembe a ku Beteli; nyanga za guwa zidzathyoka ndipo zidzagwa pansi. Onani mutuwo |
Chitatha ichi chonse tsono, Aisraele onse opezekako anatuluka kunka kumizinda ya Yuda, naphwanya zoimiritsa, nalikha zifanizo, nagamula misanje ndi maguwa a nsembe mu Yuda monse, ndi mu Benjamini, mu Efuremunso, ndi mu Manase, mpaka adaziononga zonse. Pamenepo ana onse a Israele anabwerera, yense kudziko lake ndi kumizinda yao.