Ahebri 9:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo popeza kwaikikatu kwa anthu kufa kamodzi, ndipo atafa, chiweruziro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo popeza kwaikikatu kwa anthu kufa kamodzi, ndipo atafa, chiweruziro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Munthu aliyense amafa kamodzi kokha, pambuyo pake nkumaweruzidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Popeza kunayikika kwa munthu kufa kamodzi ndipo kenaka kuweruzidwa, Onani mutuwo |