Ahebri 9:20 - Buku Lopatulika20 nati, Uwu ndi mwazi wa chipangano Mulungu adakulamulani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 nati, Uwu ndi mwazi wa chipangano Mulungu adakulamulani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pochita zimenezi adanenerera mau akuti, “Aŵa ndi magazi otsimikizira Chipangano chimene Mulungu walamula kuti mchisunge.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anati, “Awa ndi magazi a pangano limene Mulungu wakulamulirani kuti mulisunge.” Onani mutuwo |