Ahebri 12:24 - Buku Lopatulika24 ndi kwa Yesu Nkhoswe ya chipangano chatsopano, ndi kwa mwazi wa kuwaza wakulankhula chokoma choposa mwazi wa Abele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndi kwa Yesu Nkhoswe ya chipangano chatsopano, ndi kwa mwazi wa kuwaza wakulankhula chokoma choposa mwazi wa Abele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mwafika kwa Yesu, Nkhoswe yokonza za chipangano chatsopano, ndiponso mwafika ku magazi okhetsedwa, amene akutilonjeza zinthu zabwino koposa m'mene magazi a Abele ankachitira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Kwa Yesu mʼkhalapakati wa pangano latsopano, ndiponso mwafika ku magazi owazidwa amene amayankhula mawu abwino kuposa magazi a Abele. Onani mutuwo |