Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 12:20 - Buku Lopatulika

20 pakuti sanakhoze kulola cholamulidwacho. Ingakhale nyama ikakhudza phirilo, idzaponyedwa miyala;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 pakuti sanakhoza kulola cholamulidwacho. Ingakhale nyama ikakhudza phirilo, idzaponyedwa miyala;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 pakuti lidaaŵaopsa lamulo lija lakuti, “Ndi nyama yomwe ikangokhudza phirilo, iphedwe ndi miyala.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Iwo anachita mantha ndi lamulo lija lakuti, “Ngakhale nyama ikangokhudza phirilo, iphedwe ndi miyala.”

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 12:20
6 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali tsiku lachitatu, m'mawa, panali mabingu ndi zimphezi, ndi mtambo wakuda bii paphiripo, ndi liu la lipenga lolimbatu; ndi anthu onse okhala kutsasa ananjenjemera.


Pakuti ine mwa lamulo ndafa kulamulo, kuti ndikhale ndi moyo kwa Mulungu.


Pakuti onse amene atama ntchito za lamulo liwakhalira temberero; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wosakhala m'zonse zolembedwa m'buku la chilamulo, kuzichita izi.


Ndipo anati, Yehova anafuma ku Sinai, nawatulukira ku Seiri; anaoneka wowala paphiri la Parani, anafumira kwa opatulika zikwizikwi; ku dzanja lamanja lake kudawakhalira lamulo lamoto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa