Ahebri 12:19 - Buku Lopatulika19 ndi mau a lipenga, ndi manenedwe a mau, manenedwe amene iwo adamvawo anapempha kuti asawaonjezerepo mau; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 ndi mau a lipenga, ndi manenedwe a mau, manenedwe amene iwo adamvawo anapempha kuti asawaonjezerepo mau; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 limene panali kulira kwa lipenga, ndiponso kumveka kwa mau. Anthu atamva mauwo, adaapempha kuti asaŵamvenso konse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 limene pali kulira kwa lipenga, ndiponso kumveka kwa mawu. Anthu amene amamva mawuwo anapempha kuti asawayankhulenso mawu ena. Onani mutuwo |