Ahebri 12:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti simunayandikire phiri lokhudzika, ndi lakupsa moto, ndi pakuda bii, ndi mdima, ndi namondwe, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti simunayandikira phiri lokhudzika, ndi lakupsa moto, ndi pakuda bii, ndi mdima, ndi namondwe, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Inu simudachite monga Aisraele aja, amene adaafika ku chinthu chimene adaatha kuchikhudza, ndiye kuti ku Phiri la Sinai, lija linali loyaka moto, lamdima wa bii, la mphepo yamkuntho; Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Inu simunafike ku phiri limene mungathe kulikhudza, loyaka moto wa mdima bii, la mphepo yamkuntho; Onani mutuwo |