Ahebri 11:38 - Buku Lopatulika38 (amenewo dziko lapansi silinayenere iwo), osokerera m'mapululu, ndi m'mapiri, ndi m'mapanga, ndi m'mauna a dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 (amenewo dziko lapansi silinayenera iwo), osokerera m'mapululu, ndi m'mapiri, ndi m'mapanga, ndi m'mauna a dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Anthu ameneŵa, pansi pano sipadaŵayenere! Ankangoyenda m'zipululu ndi m'mapiri namabisala m'mapanga ndi m'maenje apansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Dziko lapansi silinawayenere. Anayendayenda mʼzipululu ndi mapiri, ndiponso mʼmapanga ndi mʼmaenje. Onani mutuwo |