Ahebri 11:37 - Buku Lopatulika37 anaponyedwa miyala, anachekedwa pakati, anayesedwa, anaphedwa ndi lupanga, anayendayenda ovala zikopa zankhosa, ndi zikopa zambuzi, nakhala osowa, osautsidwa, ochitidwa zoipa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 anaponyedwa miyala, anachekedwa pakati, anayesedwa, anaphedwa ndi lupanga, anayendayenda ovala zikopa zankhosa, ndi zikopa zambuzi, nakhala osowa, osautsidwa, ochitidwa zoipa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Ena adaŵapha pakuŵaponya miyala; ena adaŵacheka pakati; ndipo ena adaŵapha ndi lupanga. Ankayenda uku ndi uku atavala zikopa zankhosa kapena zambuzi, umphaŵi wokhawokha, anthu nkumaŵazunza ndi kuŵavutitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Anagendedwa miyala; anachekedwa pakati; ena anaphedwa ndi lupanga. Iwo anayendayenda atavala zikopa zankhosa ndi zikopa zambuzi, umphawi okhaokha, ozunzidwa ndi kuvutitsidwa. Onani mutuwo |