Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 11:31 - Buku Lopatulika

31 Ndi chikhulupiriro Rahabu wadama uja sanaonongeke pamodzi ndi osamverawo, popeza analandira ozonda ndi mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndi chikhulupiriro Rahabu wadama uja sanaonongeka pamodzi ndi osamverawo, popeza analandira ozonda ndi mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Pokhala ndi chikhulupiriro, Rahabu, mkazi wadama uja, sadafe nawo limodzi anthu osamvera aja, pakuti adaaŵalandira bwino azondi aja kunyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Ndi chikhulupiriro Rahabe, mkazi wadama sanaphedwe pamodzi ndi osamvera aja chifukwa analandira bwino ozonda aja ku nyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:31
10 Mawu Ofanana  

Buku la kubadwa kwa Yesu Khristu, mwana wa Davide, mwana wa Abrahamu.


ndi Salimoni anabala Bowazi mwa Rahabu; ndi Bowazi anabala Obede mwa Rute; ndi Obede anabala Yese;


Pamene anakhala nthawi, abale analawirana nao ndi mtendere amuke kwa iwo amene anawatumiza.


Ndipo adawalumbirira ayani kuti asalowe mpumulo wake?


Ndipo momwemonso sanayesedwe wolungama Rahabu mkazi wa damayo ndi ntchito kodi, popeza adalandira amithenga, nawatulutsa adzere njira ina?


Ndipo atafa Mose mtumiki wa Yehova, Yehova anati kwa Yoswa mwana wa Nuni mnyamata wa Mose,


Ndipo, Mwala wakukhumudwa nao, ndi thanthwe lophunthwitsa. Kwa iwo akukhumudwa ndi mau, pokhala osamvera, kumenekonso adaikidwako.


imene inakhala yosamvera kale, pamene kuleza mtima kwa Mulungu kunalindira, m'masiku a Nowa, pokhala m'kukonzeka chingalawa, m'menemo owerengeka, ndiwo amoyo asanu ndi atatu, anapulumutsidwa mwa madzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa