Ahebri 11:29 - Buku Lopatulika29 Ndi chikhulupiriro anaoloka Nyanja Yofiira kupita ngati pamtunda: ndiko Aejipito poyesanso anamizidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndi chikhulupiriro anaoloka Nyanja Yofiira kupita ngati pamtunda: ndiko Aejipito poyesanso anamizidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Pokhala ndi chikhulupiriro, Aisraele adaoloka Nyanja Yofiira ngati pamtunda pouma. Koma Aejipito, kuti nawonso ayesere kuwoloka, adamizidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ndi chikhulupiriro Aisraeli anawoloka Nyanja Yofiira ngati pa mtunda powuma, koma Aigupto atayesa kutero anamizidwa. Onani mutuwo |