Ahebri 10:37 - Buku Lopatulika37 Pakuti katsala kanthawi kakang'onong'ono, ndipo wakudzayo adzafika, wosachedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Pakuti katsala kanthawi kakang'onong'ono, ndipo wakudzayo adzafika, wosachedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Paja Malembo akuti, “Pangotsala kanthaŵi pang'ono chabe kuti Iye amene alikudza, afike. Sachedwa ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Pakuti nʼkanthawi kochepa chabe, Iye amene akubwera adzabwera ndipo sadzachedwa ayi. Onani mutuwo |