Ahebri 10:36 - Buku Lopatulika36 Pakuti chikusowani chipiriro, kuti pamene mwachita chifuniro cha Mulungu, mukalandire lonjezano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Pakuti chikusowani chipiriro, kuti pamene mwachita chifuniro cha Mulungu, mukalandire lonjezano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Pafunikadi kupirira, kuti muchite zimene Mulungu akufuna, kuti motero mukalandire zimene adalonjeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Nʼkofunika kuti mupirire kuti pamene muchita chifuniro cha Mulungu mudzalandire zimene Iye analonjeza. Onani mutuwo |