Ahebri 10:28 - Buku Lopatulika28 Munthu wopeputsa chilamulo cha Mose angofa opanda chifundo pa mboni ziwiri kapena zitatu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Munthu wopeputsa chilamulo cha Mose angofa opanda chifundo pa mboni ziwiri kapena zitatu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Munthu wophwanya Malamulo a Mose amaphedwa popanda nchifundo chomwe, malinga pakakhala mboni ziŵiri kapena zitatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Aliyense amene amakana malamulo a Mose amaphedwa popanda nʼchifundo chomwe, malingana pali mboni ziwiri kapena zitatu. Onani mutuwo |