Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Aefeso 6:24 - Buku Lopatulika

24 Akhale nacho chisomo onse akukonda Ambuye wathu Yesu Khristu m'chosaonongeka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Akhale nacho chisomo onse akukonda Ambuye wathu Yesu Khristu m'chosaonongeka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Onse okonda Ambuye athu Yesu Khristu ndi chikondi chosafa, Mulungu aŵadalitse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Chisomo kwa onse amene amakonda Ambuye athu Yesu Khristu ndi chikondi chosatha.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 6:24
16 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anati kwa iye, Uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi nzeru zako zonse.


ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


kwa iwo amene afunafuna ulemerero ndi ulemu ndi chisaonongeko, mwa kupirira pa ntchito zabwino, adzabwezera moyo wosatha;


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.


Pakuti ngati chivomerezocho chili pomwepo, munthu alandiridwa monga momwe ali nacho, si monga chimsowa.


Sindinena ichi monga kulamulira, koma kuyesa mwa khama la ena choonadi cha chikondi chanunso.


Mtendere ukhale kwa abale, ndi chikondi, pamodzi ndi chikhulupiriro, zochokera kwa Mulungu Atate, ndi Ambuye Yesu Khristu.


Paulo ndi Timoteo, akapolo a Yesu Khristu, kwa oyera mtima onse mwa Khristu Yesu, akukhala ku Filipi, pamodzi ndi oyang'anira ndi atumiki:


Ndipereka moni ndi dzanja langa, kwa ine Paulo. Kumbukirani zomangira zanga. Chisomo chikhale nanu.


Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale nanu.


m'zonse udzionetsere wekha chitsanzo cha ntchito zabwino; m'chiphunzitso chako uonetsere chosavunda, ulemekezeko,


Akukupatsa moni onse akukhala pamodzi ndi ine. Pereka moni kwa otikondawo m'chikhulupiriro. Chisomo chikhale ndi inu nonse.


Chisomo chikhale ndi inu nonse, Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa