Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Aefeso 6:22 - Buku Lopatulika

22 amene ndamtuma kwa inu chifukwa cha ichicho, kuti mukazindikire za kwa ife, ndi kuti akatonthoze mitima yanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 amene ndamtuma kwa inu chifukwa cha ichicho, kuti mukazindikire za kwa ife, ndi kuti akatonthoze mitima yanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ndikumtuma kwa inu kuti mudziŵe za m'mene tiliri, ndipo kuti akulimbitseni mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ine ndikumutumiza kwa inu, kuti mudziwe za moyo wathu, ndi kuti akulimbikitseni.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 6:22
7 Mawu Ofanana  

Koma ndiyembekeza mwa Ambuye Yesu kuti ndidzatumiza Timoteo kwa inu msanga, kuti inenso nditonthozeke bwino pozindikira za kwa inu.


Koma ndinayesa nkofunika kutuma kwa inu Epafrodito mbaleyo, ndiye wantchito mnzanga ndi msilikali mnzanga, ndiye mtumwi wanu, ndi wonditumikira pa chosowa changa;


kuti itonthozeke mitima yao, nalumikizike pamodzi iwo m'chikondi, kufikira chuma chonse cha chidzalo cha chidziwitso, kuti akazindikire iwo chinsinsi cha Mulungu, ndiye Khristu,


ndipo tinatuma Timoteo, mbale wathuyo ndi mtumiki wa Mulungu mu Uthenga Wabwino wa Khristu, kuti akhazikitse inu, ndi kutonthoza inu za chikhulupiriro chanu;


asangalatse mitima yanu, nakhazikitse inu mu ntchito yonse ndi mau onse abwino.


Koma Tikiko ndamtuma ku Efeso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa