Aefeso 6:22 - Buku Lopatulika22 amene ndamtuma kwa inu chifukwa cha ichicho, kuti mukazindikire za kwa ife, ndi kuti akatonthoze mitima yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 amene ndamtuma kwa inu chifukwa cha ichicho, kuti mukazindikire za kwa ife, ndi kuti akatonthoze mitima yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndikumtuma kwa inu kuti mudziŵe za m'mene tiliri, ndipo kuti akulimbitseni mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ine ndikumutumiza kwa inu, kuti mudziwe za moyo wathu, ndi kuti akulimbikitseni. Onani mutuwo |