Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Aefeso 6:15 - Buku Lopatulika

15 ndipo mutadziveka mapazi anu ndi makonzedwe a Uthenga Wabwino wa mtendere;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndipo mutadziveka mapazi anu ndi makonzedwe a Uthenga Wabwino wa mtendere;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Ndipo changu chanu polalika Uthenga Wabwino wa mtendere chikhale ngati nsapato zanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Valani Uthenga Wabwino wamtendere ku mapazi anu ngati nsapato.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 6:15
8 Mawu Ofanana  

Ha, mapazi ako akongola m'zikwakwata, mwana wamkaziwe wa mfumu! Pozinga m'chuuno mwako pakunga zonyezimira, ntchito ya manja a mmisiri waluso.


Ha, akongolatu pamapiri mapazi a iye amene adza ndi uthenga wabwino, amene abukitsa mtendere, amene adza ndi uthenga wabwino wa zinthu zabwino, amene abukitsa chipulumutso; amene ati kwa Ziyoni, Mulungu wako ndi mfumu.


Yehova, Ambuye, ndiye mphamvu yanga, asanduliza mapazi anga ngati a mbawala, nadzandipondetsa pa misanje yanga.


koma avale nsapato; ndipo anati, Musavale malaya awiri.


Koma atateyo ananena kwa akapolo ake, Tulutsani msanga mwinjiro wokometsetsa, nimumveke; ndipo mpatseni mphete kudzanja lake ndi nsapato kumapazi ake;


Ndipo adzalalikira bwanji, ngati satumidwa? Monganso kwalembedwa, Okometsetsa ndithu ali mapazi a iwo akulalikira Uthenga Wabwino wa zinthu zabwino.


Nsapato zako zikhale za chitsulo ndi mkuwa; ndipo monga masiku ako momwemo mphamvu yako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa