Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Timoteyo 4:22 - Buku Lopatulika

22 Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale nanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale nanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ambuye akhale nawe. Mulungu akukomereni mtima nonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale ndi inu nonse.

Onani mutuwo Koperani




2 Timoteyo 4:22
13 Mawu Ofanana  

ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


kwa onse a ku Roma, okondedwa a Mulungu, oitanidwa kuti akhale oyera mtima: Chisomo chikhale ndinu ndi mtendere wa kwa Mulungu Atate wathu, ndi Ambuye Yesu Khristu.


Ndipo Mulungu wa mtendere adzaphwanya Satana pansi pa mapazi anu tsopano lino. Chisomo cha Ambuye wathu Yesu Khristu chikhale ndi inu nonse.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi inu.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.


Chisomo cha Ambuye wathu Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu, abale. Amen.


Akhale nacho chisomo onse akukonda Ambuye wathu Yesu Khristu m'chosaonongeka.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu.


Ndipereka moni ndi dzanja langa, kwa ine Paulo. Kumbukirani zomangira zanga. Chisomo chikhale nanu.


chimene ena pochivomereza adalakwa ndi kutaya chikhulupiriro. Chisomo chikhale nanu.


Chisomo cha Ambuye wathu Yesu Khristu chikhale pamodzi ndi mzimu wanu. Amen.


Mupatsane moni ndi kupsompsonana kwa chikondi. Mtendere ukhale ndi inu nonse muli mwa Khristu.


Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi oyera mtima onse. Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa