Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Timoteyo 4:19 - Buku Lopatulika

19 Pereka moni kwa Prisika ndi Akwila, ndi banja la Onesifore.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Pereka moni kwa Prisika ndi Akwila, ndi banja la Onesifore.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Uperekeko moni kwa Prisika ndi Akwila ndiponso kwa a m'banja la Onesifore.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Pereka moni kwa Prisila ndi Akura pamodzi ndi banja lonse la Onesiforo.

Onani mutuwo Koperani




2 Timoteyo 4:19
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Paulo atakhala chikhalire masiku ambiri, anatsazika abale, nachoka pamenepo, napita m'ngalawa ku Siriya, pamodzi naye Prisila ndi Akwila; popeza anameta mutu wake mu Kenkrea; pakuti adawinda.


Ndipo anapeza Myuda wina dzina lake Akwila, fuko lake la ku Ponto, atachoka chatsopano ku Italiya, pamodzi ndi mkazi wake Prisila, chifukwa Klaudio analamulira Ayuda onse achoke mu Roma; ndipo Paulo anadza kwa iwo:


ndipo iye anayamba kulankhula molimba mtima m'sunagoge, koma pamene anamumva iye Prisila ndi Akwila, anamtenga, namfotokozera njira ya Mulungu mosamalitsa.


Mipingo ya ku Asiya ikupatsani moni. Akupatsani moni ndithu inu mwa Ambuye, Akwila ndi Prisika, pamodzi ndi Mpingo wa m'nyumba yao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa