2 Timoteyo 4:14 - Buku Lopatulika14 Aleksandro wosula mkuwa anandichitira zoipa zambiri: adzambwezera iye Ambuye monga mwa ntchito zake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Aleksandro wosula mkuwa anandichitira zoipa zambiri: adzambwezera iye Ambuye monga mwa ntchito zake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Aleksandro, mmisiri wa zosulasula uja adandichita zoipa kwambiri. Ambuye adzamlanga molingana ndi zimene adachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Alekisandro, mmisiri wa zitsulo anandichitira zoyipa kwambiri. Ambuye adzamubwezera pa zimene anachita. Onani mutuwo |