2 Timoteyo 3:14 - Buku Lopatulika14 Koma ukhalebe iwe mu izi zimene waziphunzira, nutsimikizika mtima nazo, podziwa amene adakuphunzitsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma ukhalebe iwe mu izi zimene waziphunzira, nutsimikizika mtima nazo, podziwa amene adakuphunzitsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma iwe, limbika pa zimene waphunzira ndipo wadziŵa kuti nzoona, paja ukuŵadziŵa amene adakuphunzitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma iwe pitiriza zimene waziphunzira ndi kuzivomereza, chifukwa ukudziwa amene anakuphunzitsa zimenezi. Onani mutuwo |