2 Timoteyo 3:13 - Buku Lopatulika13 Koma anthu oipa ndi onyenga, adzaipa chiipire, kusokeretsa ndi kusokeretsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma anthu oipa ndi onyenga, adzaipa chiipire, kusokeretsa ndi kusokeretsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 m'menemo anthu ochimwa ndi onyenga, adzanka naipiraipira, ndipo azidzanyenga ena nkumanyengedwanso iwo omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 pomwe anthu oyipa ndi onyenga adzanka nayipirayipira, kunamiza ena, iwo nʼkumanamizidwanso. Onani mutuwo |