2 Timoteyo 2:25 - Buku Lopatulika25 wolangiza iwo akutsutsana mofatsa; ngati kapena Mulungu awapatse iwo chitembenuziro, kukazindikira choonadi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 wolangiza iwo akutsutsana mofatsa; ngati kapena Mulungu awapatse iwo chitembenuziro, kukazindikira choonadi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Akhale wofatsa polangiza otsutsana naye. Mwina Mulungu angaŵapatse mwai woti atembenuke ndi kuzindikira choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Otsutsana naye awalangize mofatsa, mwina Mulungu adzawapatsa mwayi woti asinthike ndi kuzindikira choonadi. Onani mutuwo |