2 Timoteyo 2:23 - Buku Lopatulika23 Koma mafunso opusa ndi opanda malango upewe, podziwa kuti abala ndeu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma mafunso opusa ndi opanda malango upewe, podziwa kuti abala ndeu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Uzikana matsutsano opusa ndi opanda nzeru, paja ukudziŵa kuti zotere zimautsa mikangano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ukane matsutsano oyipa ndi opusa, chifukwa amayambitsa mikangano. Onani mutuwo |