2 Timoteyo 2:18 - Buku Lopatulika18 ndiwo amene adasokera kunena za choonadi, ponena kuti kuuka kwa akufa kwachitika kale, napasula chikhulupiriro cha ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ndiwo amene adasokera kunena za choonadi, ponena kuti kuuka kwa akufa kwachitika kale, napasula chikhulupiriro cha ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Iwowo adasokera nkusiya choona. Amaphunzitsa kuti kuuka kwa akufa kudachitika kale. Motero amasokoneza chikhulupiriro cha anthu ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iwowa apatuka pa choonadi. Iwo amaphunzitsa kuti kuuka kwa akufa kunachitika kale, motero amawononga chikhulupiriro cha anthu ena. Onani mutuwo |