2 Timoteyo 2:16 - Buku Lopatulika16 Koma pewa nkhani zopanda pake; pakuti adzapitirira kutsata chisapembedzo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma pewa nkhani zopanda pake; pakuti adzapitirira kutsata chisapembedzo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma nkhani zopanda pake, zosalemekeza Mulungu, uzipewe, pakuti anthu olankhula zotere adzanka nanyozeranyozera Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Upewe nkhani zopanda pake, zosalemekeza Mulungu, chifukwa anthu oyankhula zotere amanka napotokerapotokera. Onani mutuwo |