2 Timoteyo 2:13 - Buku Lopatulika13 ngati tikhala osakhulupirika, Iyeyu akhala wokhulupirika; pakuti sangathe kudzikana yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ngati tikhala osakhulupirika, Iyeyu akhala wokhulupirika; pakuti sakhoza kudzikana yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ngati ndife osakhulupirika, Iye amakhalabe wokhulupirika, pakuti sangathe kudzitsutsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ngati ndife osakhulupirika, Iye adzakhalabe wokhulupirika popeza sangathe kudzikana. Onani mutuwo |