2 Timoteyo 2:11 - Buku Lopatulika11 Okhulupirika mauwa: Pakuti ngati tidamwalira ndi Iye, tidzakhalanso moyo ndi Iye: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Okhulupirika mauwa: Pakuti ngati tidamwalira ndi Iye, tidzakhalanso moyo ndi Iye: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Aŵa ndi mau otsimikizika ndithu: “Ngati tidafa pamodzi naye, tidzakhala moyonso pamodzi naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mawu oyenera kuwadalira ndi awa: Ngati ife tinafa naye pamodzi, tidzakhalanso moyo pamodzi naye. Onani mutuwo |