Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Timoteyo 1:17 - Buku Lopatulika

17 komatu pokhala mu Roma iye anandifunafuna ine ndi khama, nandipeza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 komatu pokhala m'Roma iye anandifunafuna ine ndi khama, nandipeza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 adangoti atafika ku Roma, nkuyamba kundifunafuna mwachangu, mpaka adandipeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mʼmalo mwake, atangofika ku Roma, anandifunafuna ndipo anandipeza.

Onani mutuwo Koperani




2 Timoteyo 1:17
3 Mawu Ofanana  

Ambuye achitire banja la Onesifore chifundo; pakuti anatsitsimutsa ine kawirikawiri, ndipo sanachite manyazi ndi unyolo wanga;


(Ambuye ampatse iye apeze chifundo ndi Ambuye tsiku lijalo); ndi muja ananditumikira m'zinthu zambiri mu Efeso, uzindikira iwe bwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa