2 Timoteyo 1:11 - Buku Lopatulika11 umene ndaikikapo mlaliki, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 umene ndaikikapo mlaliki, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mulungu adandiika kuti ndikhale mlaliki, mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwino umenewu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ine ndinasankhidwa kukhala wamthenga, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwinowu. Onani mutuwo |