2 Petro 3:1 - Buku Lopatulika1 Okondedwa, iyi ndiye kalata yachiwiri ndilembera kwa inu tsopano; mwa onse awiri nditsitsimutsa mtima wanu woona ndi kukukumbutsani; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Okondedwa, uyu ndiye kalata wachiwiri ndilembera kwa inu tsopano; mwa onse awiri nditsitsimutsa mtima wanu woona ndi kukukumbutsani; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu okondedwa, kalata ndikukulemberaniyi ndi yachiŵiri. M'makalata aŵiri onseŵa ndafuna kuutsa mitima yanu kuti mukhale ndi maganizo oona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu okondedwa, iyi ndi kalata yanga yachiwiri kwa inu. Ine ndalemba makalata onse awiri kuti ndikukumbutseni ndi kukutsitsimutsani ndi cholinga choti muzilingalira moyenera. Onani mutuwo |