2 Petro 2:8 - Buku Lopatulika8 (pakuti wolungamayo pokhala pakati pao. Ndi kuona ndi kumva zao, anadzizunzira moyo wake wolungama tsiku ndi tsiku ndi ntchito zao zosaweruzika). Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 (pakuti wolungamayo pokhala pakati pao. Ndi kuona ndi kumva zao, anadzizunzira moyo wake wolungama tsiku ndi tsiku ndi ntchito zao zosaweruzika). Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Munthu wolungama uja, pokhala pakati pao, analikumva ndi kuwona machitidwe ao oipa, ndipo tsiku ndi tsiku mtima wake wolungama unkavutikadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 (Pakuti munthu wolungamayo, pokhala pakati pawo tsiku ndi tsiku ankavutika mu mtima ndi makhalidwe awo oyipa amene ankawaona ndi kuwamva). Onani mutuwo |