2 Petro 2:7 - Buku Lopatulika7 ndipo anapulumutsa Loti wolungamayo, wolema mtima ndi mayendedwe onyansa a oipa aja Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndipo anapulumutsa Loti wolungamayo, wolema mtima ndi mayendedwe onyansa a oipa aja Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma adapulumutsa Loti munthu wolungama, amene ankavutika ndi makhalidwe odzilekerera a anthu ochimwa aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma Iye anapulumutsa Loti, munthu wolungama, amene ankavutika ndi khalidwe lonyansa la anthu oyipa. Onani mutuwo |