2 Petro 2:6 - Buku Lopatulika6 ndipo pakuisandutsa makala mizinda ya Sodomu ndi Gomora anaitsutsa poigwetsa, ataiika chitsanzo cha kwa iwo akakhala osapembedza; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo pakuisandutsa makala midzi ya Sodomu ndi Gomora anaitsutsa poigwetsa, ataiika chitsanzo cha kwa iwo akakhala osapembedza; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndiponso Mulungu adaweruza mzinda wa Sodomu ndi wa Gomora naiwononga ndi moto, kuti chimenechi chikhale chitsanzo chochenjeza anthu amene adzakhale osasamala za Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mulungu anaweruza mizinda ya Sodomu ndi Gomora nayiwononga ndi moto, kuti ikhale chitsanzo cha zimene zidzachitikira anthu osapembedza Mulungu. Onani mutuwo |
Chifukwa chake, pali moyo wanga, ati Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele, Zedi Mowabu adzakhala ngati Sodomu, ndi ana a Amoni ngati Gomora, pochuluka khwisa ndi maenje a mchere, ndi bwinja losatha; otsala a anthu anga adzalanda zao, ndi otsala a mtundu wa anthu anga adzawalandira akhale cholowa chao.