2 Petro 2:5 - Buku Lopatulika5 ndipo sanalekerere dziko lapansi lakale, koma anasunga Nowa mlaliki wa chilungamo, ndi anzake asanu ndi awiri, pakulitengera dziko la osapembedza chigumula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo sanalekerera dziko lapansi lakale, koma anasunga Nowa mlaliki wa chilungamo, ndi anzake asanu ndi awiri, pakulitengera dziko la osapembedza chigumula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mulungu sadaŵalekererenso anthu akale aja, koma adangosunga Nowa yekha, mlaliki wa chilungamo, pamodzi ndi anzake asanu ndi aŵiri, pamene adadzetsa chigumula pa dziko la anthu osasamala za Iye Mulunguyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye sanalekerere dziko lapansi kalelo, koma anapulumutsa Nowa, mlaliki wa chilungamo, ndi anthu ena asanu ndi awiri atadzetsa chigumula pa dziko lapansi kwa anthu akhalidwe losapembedza Mulunguyo. Onani mutuwo |