2 Petro 1:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti iye wakusowa izi ali wakhungu, wa chimbuuzi, woiwala matsukidwe ake potaya zoipa zake zakale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti iye wakusowa izi ali wakhungu, wa chimbuuzi, woiwala matsukidwe ake potaya zoipa zake zakale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Paja munthu wopanda zimenezi ndiye kuti ngwakhungu, sangathe kuwona patali, ndipo waiŵala kuti adamtsuka machimo ake akale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma ngati wina alibe zimenezi, ndi wakhungu sangathe kuona patali, ndipo wayiwala kuti anayeretsedwa machimo ake akale. Onani mutuwo |