2 Mbiri 9:8 - Buku Lopatulika8 Wolemekezeka Yehova Mulungu wanu, wakukondwera nanu, kukuikani pa mpando wachifumu wake, mukhalire Yehova Mulungu wanu mfumu pa anthu ake; popeza Mulungu wanu anakonda Aisraele kuwakhazika kosatha, anakulongani mfumu yao, kuchita chiweruzo ndi chilungamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Wolemekezeka Yehova Mulungu wanu, wakukondwera nanu, kukuikani pa mpando wachifumu wake, mukhalire Yehova Mulungu wanu mfumu pa anthu ake; popeza Mulungu wanu anakonda Aisraele kuwakhazika kosatha, anakulongani mfumu yao, kuchita chiweruzo ndi chilungamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Atamandike Chauta, Mulungu wanu, amene wakondwera nanu, nakukhazikani pa mpando wake waufumu, kuti mukhale mfumu yotumikira Chauta, Mulungu wanu. Mulungu adakulongani ufumu kuti muzilamulira Aisraele, chifukwa choti Mulungu wanu adakonda Israele mpaka muyaya, nafuna kuti akhalepo mpaka muyaya, wakuikani kuti mukhale mfumu yake yolamulira moyenera ndi mwachilungamo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Atamandike Yehova Mulungu wanu amene wakondwera nanu nakukhazikani pa mpando wake waufumu kuti mulamulire mʼmalo mwa Yehova Mulungu wanu. Chifukwa cha chikondi cha Mulungu wanu pa Israeli, ndi khumbo lake kuti akusungeni mpaka muyaya, Iye wayika inu kukhala mfumu yawo kuti mulamulire moyenera ndi mwachilungamo.” Onani mutuwo |