2 Mbiri 9:7 - Buku Lopatulika7 Odala anthu anu, ndi odala anyamata anu awa akuima chiimirire pamaso panu, ndi kumva nzeru zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Odala anthu anu, ndi odala anyamata anu awa akuima chiimirire pamaso panu, ndi kumva nzeru zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ngodala anthu anu. Ngodala atumiki anuŵa, amene amaima pamaso panu nthaŵi zonse nkumamva nzeru zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ngodala anthu anu! Ngodala atumiki anu amene amayimirira pamaso panu nthawi zonse ndi kumamva nzeru zanu! Onani mutuwo |