Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 8:9 - Buku Lopatulika

9 Koma mwa ana a Israele Solomoni sanawayese akapolo omgwirira ntchito; koma iwowa anali anthu a nkhondo, akazembe ake aakulu, ndi akulu a magaleta ake, ndi apakavalo ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Koma mwa ana a Israele Solomoni sanawayese akapolo omgwirira ntchito; koma iwowa anali anthu a nkhondo, akazembe ake akulu, ndi akulu a magaleta ake, ndi apakavalo ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma Aisraele Solomoni sankaŵagwiritsa ntchito yaukapolo. Iwowo anali anthu ake ankhondo, nduna zake, oyang'anira magaleta ake ndi anthu ake okwera pa akavalo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Koma Solomoni sanagwiritse ntchito ya ukapolo Aisraeli; Iwo anali anthu ake ankhondo, atsogoleri a ankhondo, olamulira magaleta ndi oyendetsa magaleta ake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 8:9
7 Mawu Ofanana  

Amenewa anali akulu a akapitao a mfumu Solomoni, ndiwo mazana awiri mphambu makumi asanu akulamulira anthu.


mwa ana ao otsala m'dziko pambuyo pao, amene ana a Israele sanawathe, mwa iwowa Solomoni anawachititsa thangata mpaka lero lino.


Koma Yerusalemu wa kumwamba uli waufulu, ndiwo amai wathu.


Chifukwa chake, abale, sitili ana a mdzakazi, komatu a mfulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa