2 Mbiri 8:5 - Buku Lopatulika5 Anamanganso Betehoroni wa kumtunda, ndi Betehoroni wa kunsi, mizinda ya malinga yokhala nao malinga, zitseko, ndi mipiringidzo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anamanganso Betehoroni wa kumtunda, ndi Betehoroni wa kunsi, midzi ya malinga yokhala nao malinga, zitseko, ndi mipiringidzo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adamanganso Betehoroni wakumtunda ndi Betehoroni wakunsi, mizinda yamalinga yokhala ndi makoma, zitseko ndi mipiringidzo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Anamanganso Beti-Horoni Wakumtunda ndi Beti-Horoni Wakumunsi, mizinda yotetezedwa yokhala ndi makoma, zitseko ndi zitsulo zotchingira, Onani mutuwo |