2 Mbiri 8:16 - Buku Lopatulika16 Momwemo ntchito yonse ya Solomoni inakonzekeratu tsiku lakuika maziko a nyumba ya Yehova, mpaka anaitsiriza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Momwemo ntchito yonse ya Solomoni inakonzekeratu tsiku lakuika maziko a nyumba ya Yehova, mpaka anaitsiriza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Motero ntchito zonse za Solomoni zidatha, kuyambira pamene maziko a Nyumba ya Chauta adaikidwa mpaka pamene ntchitoyo idatha. Choncho Nyumba ya Chauta idatheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ntchito yonse ya Solomoni inachitika kuyambira tsiku limene maziko a Nyumba ya Mulungu anakhazikitsidwa mpaka kumaliza. Kotero Nyumba ya Yehova inamalizidwa. Onani mutuwo |