2 Mbiri 8:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Solomoni anamkweretsa mwana wamkazi wa Farao m'mzinda wa Davide, alowe m'nyumba imene adammangira; pakuti anati, Mkazi wanga asakhale m'nyumba ya Davide mfumu ya Israele; popeza mpopatulika pamene panafika likasa la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Solomoni anamkweretsa mwana wamkazi wa Farao m'mudzi wa Davide, alowe m'nyumba imene adammangira; pakuti anati, Mkazi wanga asakhale m'nyumba ya Davide mfumu ya Israele; popeza mpopatulika pamene panafika likasa la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Solomoni adatenga mwana wamkazi wa Farao ku mzinda wa Davide, nabwera naye ku nyumba imene adamangira mkaziyo, poti Solomoniyo ankati, “Mkazi wanga asamakhale m'nyumba ya Davide mfumu ya Israele, chifukwa chakuti malo amene kwafikira Bokosi lachipangano la Chauta ngopatulika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Solomoni anabweretsa mwana wamkazi wa Farao mu mzinda wa Davide ku nyumba yaufumu yomwe anamumangira, pakuti iye anati, “Mkazi wanga asakhale mʼnyumba yaufumu ya Davide mfumu ya Israeli, chifukwa malo amene Bokosi la Chipangano la Yehova lafikira ndi opatulika.” Onani mutuwo |